Mawu Amunsi
a Cioneka kuti Arimateya ni malo amodzi-modzi amene anali kuchedwa Rama, dela limene masiku ano amati Rentis (Rantis). Kumeneku ndiye kunali kwawo kwa mneneli Samueli. Delali linali pamtunda wa makilomita 35 kum’poto cakum’madzulo kwa Yerusalemu.—1 Sam. 1:19, 20.