LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Anthu ambili sadziŵa kuti mau opezeka m’ma Baibo ena pa Yohane 7:53, Yohane 8:11 ni owonjezela cabe, ndipo sali mbali ya Mau a Mulungu ouzilidwa. Cifukwa ca mau a pa lembali, anthu ena amakamba kuti popeza tonse ndise ocimwa, sitiyenela kumuimba mlandu munthu akacita cigololo. Koma Mulungu anapatsa mtundu wa Aisiraeli lamulo lakuti: “Mwamuna akapezeka akugona ndi mkazi wa mwiniwake, mwamuna ndi mkaziyo, onsewo azifela pamodzi.”—Deut. 22:22.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani