LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Buku lofalitsidwa na bungwe lina la zaumoyo ku Britain linati: “Ma IUD okhala na kopa yambili ni odalilika ngako cakuti ciŵelengelo ca azimayi amene satenga mimba ngati amaseŵenzetsa njilayi cimapitilila 99 pelesenti. Izi zitanthauza kuti ciŵelengelo ca azimayi amene angatenge mimba pa caka ngati aseŵenzetsa ma IUD aconco sicifika ngakhale 1 pelesenti. Koma ma IUD okhala na kopa yocepa, amakhalanso ocepelako mphamvu.”—England’s National Health Service.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani