LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Liu lakuti “abale” lingaphatikizepo akazi mumpingo. Paulo anachula Akhristu a ku Roma amene anawalembela kalata kuti “abale.” Koma mwacionekele mu mpingowo munalinso alongo, ndipo ena anawachula maina awo. (Aroma 16:1, 3, 6, 12) Kwa nthawi yaitali, Nsanja ya Mlonda yakhala ikuchula Akhristu oona kuti ‘abale na alongo.’

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani