LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

b N’zoonekelatu kuti pa anthu amene adzapulumuka Aramagedo, ena adzakhala olemala. Pamene Yesu anali pa dziko lapansi, anacilitsa anthu okhala na “zofooka zilizonse.” Izi zinacitila cithunzi zimene iye adzacita kwa opulumuka Aramagedo, osati kwa oukitsidwa. (Mat. 9:35) Mwacidziŵikile, akufa adzaukitsidwa ali na mathupi athanzi, opanda cilema ciliconse.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani