LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Akatswili ofukula zinthu zakale anapeza zakudya zambili m’matongwe a ku Yeriko. Izi zigwilizana na zimene Baibo imakamba, zakuti Aisiraeli sanazinge mzinda wa Yeriko kwa nthawi yaitali. Olo kuti Aisiraeli sanaloledwe kudya zakudya za mu mzindawo, imeneyi inali nthawi yoyenelela yakuti iwo alande dziko la Kanani cifukwa inali nyengo yokolola, ndipo m’minda munali zakudya zambili.—Yos. 5:10-12.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani