LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Kukamba zoona, ngakhale anthu amene amakanitsitsa kutengela nzelu za ena, sangapeweletu kusonkhezeledwa na maganizo a anthu ena. Kaya ni poganizila nkhani yaikulu monga ya ciyambi ca moyo, kapena pa nkhani yaing’ono monga ya kusankha covala cakuti avale, munthu aliyense amasonkhezeledwako ndithu na maganizo a ena. Komabe, tili na ufulu wosankha kuti tidzatengela maganizo a ndani.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani