LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a M’lemba la caka ca 2019, muli mfundo zitatu zimene zingatithandize kukhalabe odekha pamene zinthu zoipa zikucitika m’dziko, kapena pamene takumana na mavuto. M’nkhani ino, tidzakambilana mfundo zimenezo. Kucita izi kudzatithandiza kuti tisamakhale na nkhawa kwambili, koma kuti tizidalila Yehova. Muzisinkha-sinkha lemba la caka limeneli. Liloŵezeni pa mtima ngati n’kotheka. Mukatelo, lidzakuthandizani kupilila mavuto amene mudzakumana nawo kutsogolo.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani