LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Mofanana na wamasalimo Davide, tonse timakonda Yehova komanso timafunitsitsa kum’tamanda. Pamene tasonkhana na Akhristu anzathu, timakhala na mwayi wapadela woonetsa kuti timakonda Mulungu. Komabe, ena a ife zimativuta kupeleka ndemanga pamisonkhano. Ngati mumayopa kupeleka ndemanga pa misonkhano, nkhani ino idzakuthandizani kudziŵa zimene zimakupangitsani kuyopa. Komanso idzafotokoza zimene mungacite kuti mucepetse vuto limeneli.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani