LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Kodi tidzakhalabe okhulupilika kwa Yehova, kapena tidzalola Satana kutikopa mpaka kusiya kutumikila Mulungu? Ngati tiyesetsa kuteteza mtima wathu, tingakhalebe okhulupilika kwa Mulungu, olo titakumana na mayeselo aakulu bwanji. Koma kodi “mtima” umenewu n’ciani? N’ciani cimene Satana amacita pofuna kuipitsa mtima wathu? Nanga tingauteteze bwanji? M’nkhani ino, tidzakambilana mafunso ofunika kwambili amenewa.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani