LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Kodi kukhala na mtima wamphumphu kumatanthauzanji? N’cifukwa ciani Yehova amaona kuti kukhala na mtima wamphumphu n’kofunika kwambili? Nanga kukhala na mtima wotelo kuli na ubwino wanji kwa ife? Nkhani ino idzafotokoza mayankho a m’Baibo pa mafunso amenewa. Idzafotokozanso zimene zingatithandize kuti tsiku lililonse tizicita zinthu zoonetsa kuti tili na mtima wamphumphu. Ndipo tikatelo, tidzadalitsidwa kwambili.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani