LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Tonsefe sitinabadwe na khalidwe la kufatsa. Timacita kuliphunzila. Cimakhala copepuka kukhala ofatsa ngati ticita zinthu ndi anthu amtendele. Koma ngati ticita zinthu ndi anthu onyada, kukhala ofatsa kungakhale kovuta. M’nkhani ino, tidzakambilana zinthu zina zimene tiyenela kusamala nazo, kuti tikhalebe na khalidwe labwino limeneli la kufatsa.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani