LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

b MAWU OFOTOKOZEDWA: Tikanena kuti kucitila mwana zolaula, titanthauza kuti munthu wamkulu wagwilitsila nchito mwana kukhutilitsa cilakolako cake ca kugonana. Zingaphatikizepo kugona naye, kumugona mkamwa kapena kumbuyo, kum’sisita malisece, maŵele, kapena matako, kapenanso kumucita zinthu zina zosayenela. Nthawi zambili ana amene amacitilidwa zolaula na atsikana, koma palinso anyamata ambili amene amacitilidwa nkhanza zimenezi. Cinanso, ngakhale kuti ambili amene amacitila ana zolaula ni amuna, palinso akazi ena amene amacita zimenezi.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani