Mawu Amunsi
a Satana ni katswili posoceletsa anthu. Iye wasoceletsa anthu ambili mwa kuwapangitsa kuona kuti ali pa ufulu, pamene m’ceni-ceni wawagwila kukhala akapolo ake. M’nkhani ino, tidzakambilana macenjela angapo amene Satana amaseŵenzetsa posoceletsa anthu.