Mawu Amunsi
a Nkhawa yopambanitsa kapena yokhalitsa, ingatifooketse na kutibweletsela matenda. Kodi Yehova angatithandize bwanji kuthetsa nkhawa? M’nkhani ino, tikambilana mmene Yehova anathandizila Eliya kuthetsa nkhawa zake. Tikambilananso zitsanzo zina za m’Baibo, zoonetsa zimene tingacite kuti Yehova atithandize tikakhala na nkhawa.