Mawu Amunsi
a Nchito yaikulu ya mpingo wacikhristu ni kuthandiza anthu kuti akhale ophunzila a Khristu. M’nkhani ino, muli malangizo amene adzatithandiza pogwila nchito imeneyi.
a Nchito yaikulu ya mpingo wacikhristu ni kuthandiza anthu kuti akhale ophunzila a Khristu. M’nkhani ino, muli malangizo amene adzatithandiza pogwila nchito imeneyi.