Mawu Amunsi
b “Chitawala” ni liwu locokela ku Ciswahili, limene limatanthauza “kulamulila kapena kutsogolela.” Chitawala linali gulu landale, ndipo colinga cake cinali kumenyela ufulu wodzilamulila kucoka m’manja mwa dziko la Belgium. Anthu a Chitawala anali kutenga mabuku a Mboni za Yehova, kuwaŵelenga, na kumawagaŵila, ndipo anali kupotoza ziphunzitso za m’Baibo, n’colinga cakuti zigwilizane na mfundo zawo zandale, miyambo ya zamizimu, komanso makhalidwe ena oipa.