Mawu Amunsi
a Masiku ano, pa dzikoli pali anthu ambili osapembedza kuposa kale lonse. Ena timakumana nawo m’gawo lathu pamene tili mu ulaliki. Nkhani ino, idzafotokoza mmene tingalalikile coonadi ca m’Baibo kwa anthu otelo. Idzafotokozanso mmene tingawathandizile kuti ayambe kukhulupilila Yehova Mulungu na mawu ake, Baibo.