LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

f Tifunikanso kupewa kuseŵenzetsa malo a zosangalatsa ocilikizidwa na cipembedzo conama, kapena kugwilizana na mabungwe monga ma youth camps, amene ni ogwilizana na cipembedzo conama. Mabungwe amenewo angaphatikizepo la YMCA (Young Men’s Christian Association), komanso la YWCA (Young Women’s Christian Association). Anthu a m’mabungwe amenewa angakambe kuti zocita zawo si zacipembedzo. Koma zoona zake n’zakuti, mabungwewa amalimbikitsa mfundo na zolinga zacipembedzo.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani