Mawu Amunsi
a DZIŴANI IZI: Mbali yakuti “Fufuzani” mungasankhe kuikambilana pophunzila kapena ayi. Ngakhale n’telo, pezani nthawi yoiŵelenga kapena kuonelela vidiyo iliyonse pamene mukonzekela. Mukatelo, mudzadziŵa zimene zingam’cititse cidwi wophunzila wanu na kum’thandiza. Buku la pacipangizo lili na malinki a mavidiyo komanso nkhani zina.