Mawu Amunsi
b Pa cifukwa cimeneci, sitingakambenso kuti Mfumu Yaikulu ya Roma, Uleliya (wolamulila kuyambila mu 270-275 C.E.) anali “mfumu ya kumpoto.” Komanso, sitingakambe kuti Mfumukazi Zenobia (wolamulila kuyambila mu 267-272 C.E.) anali “mfumu ya kum’mwela.” Izi zasintha mfundo zimene zili m’buku lakuti Samalani Ulosi wa Danieli! macaputa 13 na 14.