LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Tikukhala m’dziko lolamulidwa na Satana, tate wake wa bodza. Conco zingakhale zovuta kwambili kuyenda m’coonadi. Umu ni mmenenso zinalili kwa Akhristu a m’nthawi ya atumwi. Pofuna kuthandiza Akhristu amenewo na ife masiku ano, Yehova anauzila mtumwi Yohane kulemba makalata atatu. Mfundo za m’makalata amenewa zingatithandize kudziŵa zinthu zimene zingatilepheletse kuyendabe m’coonadi. Komanso zingatithandize kudziŵa zimene tingacite kuti tisagonje ku zinthu zimenezo.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani