LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

c MAWU OFOTOKOZELA ZITHUNZI: Zithunzi zitatuzo zionetsa zimene zimacitika msonkhano wa pa mpingo usanayambe, uli mkati, komanso ukatha. Cithunzi coyamba: Mkulu apatsa mlendo moni mwacimwemwe, m’bale wacinyamata akonza zolankhulila, ndiponso mlongo aceza na mlongo wokalamba. Caciŵili: Acikulile na acicepele omwe, akupeleka ndemanga pa Phunzilo la Nsanja ya Mlonda. Cacitatu: Okwatilana athandiza kuyeletsa mu Nyumba ya Ufumu. Mayi athandiza mwana wake kuika copeleka m’bokosi la zopeleka. M’bale wacinyamata asamalila mabuku, komanso m’bale alimbikitsa mlongo wokalamba.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani