Mawu Amunsi
b Kuti mudziŵe zambili, onani mutu 9 m’buku lakuti Baibulo—Kodi Ndilo Mawu a Mulungu Kapena a Munthu? lofalitsidwa na Mboni za Yehova. Bukuli lipezekanso pa webusaiti yathu ya www.jw.org. Pitani ku Chichewa pa LAIBULALE > MABUKU NDI ZINTHU ZINA.