LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Yesu ananena kuti ophunzila ake adzadziŵika na cikondi cimene amaonetsana pakati pawo. Tonsefe timayesetsa kuonetsa cikondi cimeneci. Tiyenela kukulitsa cikondi cathu pa abale athu mwa kuwakonda mmene timakondela anthu a m’banja lathu lakuthupi. Nkhani ino, idzatithandiza kukhala na cikondi ceni-ceni, na kuyesetsa kucionetsa kwa abale na alongo athu a m’cikhulupililo.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani