Mawu Amunsi
b Pa utumiki wake, Yesu nthawi zina anali kukamba zinthu kapena kufunsa mafunso amene sanali kuonetsa mmene iye anali kumvelela. Anali kucita izi na colinga cakuti ayambitse makambilano na otsatila ake.—Maliko 7:24-27; Yoh. 6:1-5; onani Nsanja ya Olonda ya October 15, 2010, tsamba. 4-5.