LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

c MAWU OFOTOKOZELA ZITHUNZI: (kucoka pamwamba kupita pansi): Mwamuna na mkazi wake akulalikila m’dela limene n’zovuta kupeza anthu panyumba. Mwininyumba woyamba ali ku nchito, waciŵili ali ku cipatala, ndipo wacitatu akugula zinthu m’sitolo. Ofalitsawo afikila mwininyumba woyamba pa nthawi ina pa tsikulo. Akambilana na mwininyumba waciŵili pamene akucita ulaliki wapoyela pafupi na cipatala. Iwo akambilana na mwininyumba wacitatu mwa kum’tumila foni.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani