LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Cifukwa ca kupanda ungwilo, tingakambe kapena kucita zinthu zimene zingakhumudwitse abale na alongo athu. Kodi zaconco zikacitika timacita ciani? Kodi timayesetsa kukonzanso ubale wathu? Kodi timapepesa mwamsanga? Kapena mumakhala na maganizo akuti ‘ilo ni vuto lawo osati langa?’ Kapena timakhumudwa msanga na zimene ena angakambe kapena kucita? Kodi timadzilungamitsa pa zimene tacita mwa kukamba kuti ndiye mmene tilili, n’cibadwa cathu? Kapena timaona zimene tacita monga cifooko cimene tiyenela kugwililapo nchito?

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani