LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

c MAWU OFOTOKOZELA ZITHUNZI: Onani mmene kuphunzila Baibo na munthu kungam’thandizile kupanga masinthidwe mu umoyo wake: Poyamba munthu uyu aoneka kuti moyo wake ulibe colinga, ndipo sadziŵa Yehova. Ndiyeno Mboni za Yehova zakumana naye pamene zikulalikila, ndipo wavomela kuphunzila Baibo. Zimene waphunzilazo zam’thandiza kuti adzipatulile na kubatizika. M’kupita kwanthawi, iyenso wayamba kuthandiza ena kukhala ophunzila a Yesu. Pamapeto pake, onse akukondwela na moyo m’paradaiso.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani