LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Aliyense wa ife amakumana na mavuto osiyanasiyana. Pali pano, palibe njila yothetsela ambili mwa mavuto amenewa. Timangofunika kuwapilila. Koma sitili tekha. Yehova nayenso akupilila zambili. M’nkhani ino, tikambilane zinthu 9 zimene Yehova wakhala akupilila. Tikambilanenso zimene zatheka cifukwa ca kupilila kwa Yehova, komanso zimene tingaphunzilepo pa citsanzo cake ca kupilila.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani