LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Timakondwela anthu akalandila uthenga wathu, koma timakwinyilila akakana uthengawo. Bwanji ngati munthu amene mumaphunzila naye Baibo sapita patsogolo? Kapena bwanji ngati mukalibe kuthandizapo munthu mpaka kufika pobatizika? Kodi muyenela kuganiza kuti mwalephela nchito yopanga ophunzila? M’nkhani ino, tiona mmene tingakhalile opambana komanso acimwemwe mu ulaliki, kaya anthu amvetsele kapena ayi.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani