LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Yehova timam’konda kwambili, ndipo timafuna kum’kondweletsa. Iye ni woyela, ndipo amafuna kuti alambili ake akhale oyela. Kodi n’zotheka anthu opanda ungwilo kukhala oyela? Inde n’zotheka. Kuganizila mofatsa malangizo amene mtumwi Petulo anapatsa Akhristu anzake, komanso malamulo amene Yehova anapatsa Aisiraeli, kudzatithandiza kuona mmene tingakhalile oyela m’makhalidwe athu onse.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani