LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Pamene Yesu anakamba kuti nkhosa zake zidzamva mawu ake, anatanthauza kuti ophunzila ake adzamvela ziphunzitso zake, na kuziseŵenzetsa pa umoyo wawo. M’nkhani ino, tikambilane ziphunzitso ziŵili za Yesu zofunika kwambili, zimene ni kuleka kudela nkhawa zinthu zakuthupi, komanso kuleka kuweluza ena. Tikambilanenso mmene tingaseŵenzetsele malangizo a Yesu amenewa.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani