Mawu Amunsi
a Tonsefe tingapindule na zitsanzo za ena mu mpingo. Koma tiyenela kupewa kudzilinganiza na iwo. Nkhani ino, itithandiza kukhalabe acimwemwe, na kupewa kudzikuza kapena kulefuka cifukwa coyelekezela nchito zathu na nchito za ena.
a Tonsefe tingapindule na zitsanzo za ena mu mpingo. Koma tiyenela kupewa kudzilinganiza na iwo. Nkhani ino, itithandiza kukhalabe acimwemwe, na kupewa kudzikuza kapena kulefuka cifukwa coyelekezela nchito zathu na nchito za ena.