Mawu Amunsi
b MAWU OFOTOKOZELA CITHUNZI: M’bale akutumikila pa Beteli ali wacinyamata. Pambuyo pake, anakwatila ndipo anayamba upainiya na mkazi wake. Atakhala na ŵana, anawaphunzitsa kulalikila. Tsopano m’zaka zake zaukalamba, akupitiliza kucita zimene angathe pocita ulaliki wa m’makalata.