LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

e MAWU OFOTOKOZELA ZITHUNZI: John amaseŵenza ovataimu. Iye safuna kukhumudwitsa abwana ake. Conco, nthawi iliyonse abwana ake akamuuza kuti agwile ovataimu John amavomela. Koma madzulo amodzi-modziwo, Tom, amene ni mtumiki wothandiza, wapita ku ulendo waubusa na mkulu wina. Kumbuyoku, Tom anauza abwana ake kuti madzulo alionse amapatula nthawi yocita zinthu zokhudza kulambila Yehova.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani