LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Kucita mantha n’cibadwa, ndipo kungatiteteze ku zinthu zoopsa. Koma kukhala na mantha osayenela si kwabwino cifukwa kungatigwetsele m’mavuto. Motani? Satana angagwilitsile nchito mantha amenewo kuti atipangitse kupanga cisankho colakwika. Conco, tiyenela kuyesetsa kugonjetsa mantha otelowo. Kodi n’ciyani cingatithandize? Monga tionele m’nkhani ino, tikakhulupilila kuti Yehova ali ku mbali yathu komanso kuti amatikonda, tidzakwanitsa kugonjetsa mantha alionse.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani