LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Padziko lonse lapansi, mamiliyoni a anthu ophatikizapo amuna, akazi, ndiponso ana akulalikila uthenga wabwino mokangalika. Kodi ndinu mmodzi wa iwo? Ngati n’telo, ndiye kuti mukugwila nchito pansi pa uyang’anilo wa Ambuye wathu, Yesu Khristu. M’nkhani ino, tikambilane umboni woonetsa kuti Yesu ndiye akutsogolela nchito yolalikila masiku ano. Tikamaiganizila mfundo imeneyi, tidzakhala ofunitsitsa kum’tumikilabe Yehova motsogoleledwa na Khristu.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani