Mawu Amunsi
a Timafunika thandizo la Yehova kuti tikwanitse kupilila mavuto amene timakumana. Nkhani ino itithandiza kuona kuti maso a Yehova alidi pa anthu ake. Iye amaona mavuto amene timakumana nawo aliyense payekha, ndipo amatipatsa zofunikila kuti tithane nawo mavutowo.