Mawu Amunsi
a Umoyo m’dzikoli ni wovuta. Abale na alongo athu amakumana na mavuto osiyana-siyana. Tingakhale dalitso kwa iwo ngati timapeza mipata yakuti tiwalimbikitse. Kukambilana citsanzo mtumwi Paulo kutithandiza pa nkhani imeneyi.
a Umoyo m’dzikoli ni wovuta. Abale na alongo athu amakumana na mavuto osiyana-siyana. Tingakhale dalitso kwa iwo ngati timapeza mipata yakuti tiwalimbikitse. Kukambilana citsanzo mtumwi Paulo kutithandiza pa nkhani imeneyi.