Mawu Amunsi
d MAWU OFOTOKOZELA CITHUNZI: Mkulu akulimbikitsa m’bale amene cikhulupililo cake cafooka. Akuonetsa m’baleyo mapikica a Sukulu ya Utumiki Waupainiya imene analoŵela pamodzi kumbuyoko. Mapikicawo am’kumbutsa nthawi pamene anali kusangalala na utumiki. M’baleyo wayamba kulakalaka cimwemwe cimene anali naco pamene anali kutumikila Yehova. Potsilizila pake, iye akuyambanso kucita zauzimu.