LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a N’kovuta kupeza anthu acilungamo m’dziko loipali. Ngakhale n’telo, masiku ano pali anthu mamiliyoni amene akutsatila njila yacilungamo. Ndipo sitikukayika kuti ndinu mmodzi wa iwo. Mumatsatila njila ya cilungamo cifukwa mumakonda Yehova, amene amakonda cilungamo. Kodi tingacite ciyani kuti tizilikonda kwambili khalidwe labwino limeneli? M’nkhani ino, tione kuti cilungamo n’ciyani, komanso mmene timapindulila tikamacikonda cilungamo. Tikambilanenso masitepe amene tingatenge kuti tizilikonda kwambili khalidwe limeneli.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani