LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Anthu ambili amavutika kucipeza cimwemwe ceniceni cifukwa amacifuna-funa kolakwika. Iwo amaona kuti angacipeze m’zosangulutsa, cuma, kuchuka, kapena mwa kukhala na mphamvu. Koma pamene Yesu anali padziko lapansi, anauza anthu mmene angacipezele cimwemwe ceniceni. Ndiye cifukwa cake m’nkhani ino, tikambilane zinthu zitatu zimene zingatithandize kupeza cimwemwe ceniceni.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani