Mawu Amunsi
a Nzelu imene Yehova amapeleka, ni yofunika kuposa cinthu cina ciliconse m’dzikoli. M’nkhani ino, tikambilane mawu ofanizila ocititsa cidwi opezeka m’buku la Miyambo, akuti nzelu imakhalila kufuula mumsewu. Tikambilanenso mmene tingapezele nzelu yeniyeni, cifukwa cake anthu ena amatseka makuti kuti asamvetsele nzelu yeniyeni, komanso mmene timapindulila tikamamvetsela nzeluyo.