LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

b KUFOTOKOZELA MAWU ENA: “Paradaiso wauzimu” ni mkhalidwe wacitetezo cauzimu umene tilimo mmene tikulambila Yehova mogwilizana. M’paradaiso wauzimu ameneyu tili na cakudya cauzimu camwana alilenji cosaipitsidwa na mabodza a zipembedzo zonyenga. Cina, timagwilanso nchito yokhutilitsa yolalikila uthenga wabwino wa Ufumu wa Mulungu. Tili pa ubale wolimba na Yehova, ndiponso timakhala mwamtendele na abale komanso alongo athu acikondi amene amatithandiza kupilila mwacimwemwe zovuta za paumoyo. Timaloŵa m’paradaiso wauzimu ameneyu tikayamba kulambila Yehova m’njila yoyenela, komanso pamene ticita zonse zotheka kuti titengele citsanzo cake.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani