Mawu Amunsi
a Lemba la caka ca 2023 n’lolimbitsa cikhulupililo. N’lakuti: “Mawu anu onse ndi coonadi cokha-cokha.” (Sal. 119:160) Mosakayika, mukuvomeleza mfundoyi. Koma anthu ambili sakhulupilila kuti Baibo ili na coonadi, ndiponso kuti lingatipatse citsogozo codalilika. M’nkhani ino, tikambilane maumboni atatu amene tingaseŵenzetse potsimikizila anthu oona mtima, kuti angaikhulupililedi Baibo na upangili wake.