LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Lemba la caka ca 2023 n’lolimbitsa cikhulupililo. N’lakuti: “Mawu anu onse ndi coonadi cokha-cokha.” (Sal. 119:160) Mosakayika, mukuvomeleza mfundoyi. Koma anthu ambili sakhulupilila kuti Baibo ili na coonadi, ndiponso kuti lingatipatse citsogozo codalilika. M’nkhani ino, tikambilane maumboni atatu amene tingaseŵenzetse potsimikizila anthu oona mtima, kuti angaikhulupililedi Baibo na upangili wake.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani