Mawu Amunsi
a Pa Ciŵili, April 4, 2023, anthu mamiliyoni padziko lonse lapansi adzasonkhana kuti acite Cikumbutso ca imfa ya Khristu. Ena kudzakhala kuyamba kupezekapo. Ndipo ena amene akhala Mboni zozilala kwa zaka zambili nawonso adzapezekapo. Ena adzakhala atagonjetsa zopinga zina kuti akapezeke pa Cikumbutso. Kaya zinthu zili motani pa umoyo wanu, dziŵani kuti Yehova adzakondwela kwambili poona kuti mwayesetsa kuti mupezekepo.