LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Pa Ciŵili, April 4, 2023, anthu mamiliyoni padziko lonse lapansi adzasonkhana kuti acite Cikumbutso ca imfa ya Khristu. Ena kudzakhala kuyamba kupezekapo. Ndipo ena amene akhala Mboni zozilala kwa zaka zambili nawonso adzapezekapo. Ena adzakhala atagonjetsa zopinga zina kuti akapezeke pa Cikumbutso. Kaya zinthu zili motani pa umoyo wanu, dziŵani kuti Yehova adzakondwela kwambili poona kuti mwayesetsa kuti mupezekepo.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani