Mawu Amunsi
b Anthu a zipembedzo zimenezo amakhulupilila kuti pa nthawi ya mwambo umenewu, mkate na vinyo zimasandulika n’kukhala thupi lenileni, komanso magazi enieni a Khristu. Iwo amaona kuti thupi la Yesu na magazi ake zimapelekedwa nsembe nthawi iliyonse mwambowu ukamacitika.