Mawu Amunsi
a Baibo imatithandiza kumuyandikila Yehova. Kodi tingaphunzile ciyani m’buku lopatulika limenelo zokhudza nzelu za Mulungu, cilungamo cake, na cikondi cake? Zimene timaphunzila zingatithandize kukulitsa ciyamikilo cathu pa Mawu a Mulungu. Zingatithandizenso kuona kuti Baibo ilidi mphatso yocokela kwa Atate wathu wakumwamba.