Mawu Amunsi
c Mariya anali kuwadziŵa bwino Malemba, ndipo anali kuwagwila mawu. (Luka 1:46-55) Mwacionekele, Yosefe na Mariya analibe ndalama zokwanila zogulila mipukutu yawo-yawo ya Malemba. Iwo ayenela kuti anali kumvetsela mwachelu Mawu a Mulungu akamaŵelengedwa m’Sunagoge. Ndipo izi zinali kuwathandiza kuwakumbukila pambuyo pake.